Ezra 10:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nawu mndandanda wa ansembe amene adaakwatira akazi achilendo: Pa banja la Yesuwa ndi abale ake, ana a Yozadaki, panali aŵa: Maaseiya, Eliyezere, Yaribu ndi Gedaliya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anapeza mwa ana a ansembe odzitengera akazi achilendo, ndiwo a ana a Yesuwa mwana wa Yozadaki, ndi abale ake Maaseiya, ndi Eliyezere, ndi Yaribu, ndi Gedaliya.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nawu mʼndandanda wa ansembe amene anakwatira akazi achikunja: Pa banja la Yesuwa ndi abale ake, ana a Yozadaki, panali awa: Maaseiya, Eliezara, Yaribu ndi Gedaliya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anapeza mwa ana a ansembe odzitengera akazi acilendo, ndiwo a ana a Yesuwa mwana wa Yozadaki, ndi abale ace Maseya, ndi Eliezere, ndi Yaribu, ndi Gedaliya.