Ezra 10:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwo adatsimikiza zochotsa akazi ao, ndipo adapereka nkhosa yamphongo yopepesera machimo ao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anaimika dzanja lao kuti adzachotsa akazi ao; ndipo popeza adapalamuladi, anapereka nsembe nkhosa yamphongo ya zoweta pa kupalamula kwao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anatsimikiza zochotsa akazi awo ndipo chifukwa cha kulakwa kwawo aliyense anapereka nkhosa yayimuna ngati nsembe yopepesera machimo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anaimika dzanja lao kuti adzacotsa akazi ao; ndipo popeza adaparamuladi, anapereka nsembe nkhosa yamphongo ya zoweta pa kuparamula kwao.