Ezra 10:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pa banja la Imara panali Hanani ndi Zebadiya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi a ana a Imeri: Hanani ndi Zebadiya.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pa banja la Imeri panali awa: Hanani ndi Zebadiya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi a ana a Imeri: Hanani ndi Zebadiya.