Ezra 2:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amuna a ku Mikimasi, 122.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anthu a Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu aamuna a ku Mikimasi — 122
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anthu a Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.