Ezra 2:43 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Antchito a ku Nyumba ya Mulungu anali aŵa: a banja la Ziha, a banja la Hasufa, a banja la Tabaoti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anetini: ana a Ziha, ana a Hasufa, ana a Tabaoti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Otumikira ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anetini: ana a Ziha, ana a Hasufa, ana a Tabaoti,