Ezra 2:60 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
A banja la Delaya, a banja la Tobiya ndi a banja la Nekoda, 642.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ana a Delaya, ana a Tobiya, ana a Nekoda, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya, ndi zidzukulu za Nekoda. Onse pamodzi anali — 652.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ana a Delaya, ana a Tobiya, ana a Nekoda, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.