Galatians 1:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mudamva za mayendedwe anga kale pamene ndinali m'Chiyuda. Ndinkazunza Mpingo wa Mulungu koopsa, ndipo ndinkayesetsa kuuwonongeratu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti mudamva za makhalidwe anga kale mwa Chiyuda, kuti ndinalondalonda Mpingo wa Mulungu koposa, ndi kuupasula,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti inu munamva za moyo wanga wakale mʼChiyuda, mmene ndinkazunzira mpingo wa Mulungu koopsa ndi kuyesetsa kuwuwononga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti mudamva za makhalidwe anga kale mwa Ciyuda, kuti ndinalondalonda Mpingo wa Mulungu koposa, ndi kuupasula,