Galatians 1:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Sindidapite ngakhalenso ku Yerusalemu kwa anthu amene anali atumwi kale ine ndisanakhale mtumwi. Koma ndidapita ku Arabiya kenaka nkubwereranso ku Damasiko.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kapena kukwera kunka ku Yerusalemu sindinankako kwa iwo amene anakhala atumwi ndisanakhale mtumwi ine, komatu ndinamuka ku Arabiya, ndipo ndinabweranso ku Damasiko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine sindinapite ku Yerusalemu kukaonana ndi amene anali atumwi ine ndisanakhale mtumwi. Mʼmalo mwake nthawi yomweyo ndinapita ku Arabiya ndi kubwereranso ku Damasiko.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
kapena kukwera kunka ku Yerusalemu sindinankako kwa iwo amene anakhala atumwi ndisanakhale mtumwi ine, komatu ndinamuka ku Arabiya, ndipo ndinabweranso ku Damasiko.