Galatians 1:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikulumbira pamaso pa Mulungu kuti zimene ndikukulemberanizi ndi oona, sindikunama ai.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo izi ndikulemberani inu, taonani, pamaso pa Mulungu sindinama ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndikutsimikizira inu pamaso pa Mulungu kuti zimene ndikukulemberani si zonama ayi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo izi ndikulemberani inu, taonani, pamaso pa Mulungu sindinama ine.