Galatians 2:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adangopempha chokhachi kuti tisaleke kukumbukira anthu ao aumphaŵi. Ndipotu chimenechi ndicho ndakhala ndikuchita moikapo mtima.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pokhapo kuti tikumbukire aumphawi; ndicho chomwe ndinafulumira kuchichita.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chimene iwo anapempha ndi chakuti ife tipitirize kukumbukira osauka, chinthu chimene ine ndinali okonzeka kuchichita.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pokhapo kuti tikumbukile aumphawi; ndico comwe ndinafulumira kucicita.