Galatians 2:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma kunena za aja ankaŵayesa atsogoleriŵa, (kaya analidi atsogoleri kaya, ndilibe nazo kanthu. Mulungu sakondera paja), iwowo sadaonjeze kanthu kena koti ndilalike.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma iwo akuyesedwa ali kanthu (ngati anali otani kale, kulibe kanthu kwa ine; Mulungu salandira nkhope ya munthu) iwo omvekawo sanandionjezera ine kanthu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma kunena za aja ankaoneka ngati ofunika kwambiri, chimene iwo anali sichisintha kanthu kwa ine; chifukwa Mulungu alibe tsankho, iwowo sanawonjezepo kanthu pa uthenga wanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma iwo akuyesedwa ali kanthu (ngati anali otani kale, kulibe kanthu kwa ine; Mulungu salandira nkhope ya munthu) iwo omvekawo sanandionjezera ine kanthu;