Galatians 2:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Makamaka adaaona kuti Mulungu adandipatsa ine ntchito ya kulalika Uthenga Wabwino kwa anthu osakhala Ayuda, monga momwe adapatsira Petro ntchito ya kuulalika kwa Ayuda.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
koma pena, pakuona kuti anaikiza kwa ine Uthenga Wabwino wa kusadulidwa, monga kwa Petro Uthenga Wabwino wa mdulidwe
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Makamaka anaona kuti ine ndinapatsidwa ntchito yolalikira Uthenga Wabwino kwa anthu a mitundu ina monga momwe Petro anapatsidwa ntchito yolalikira Uthenga Wabwino kwa Ayuda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
koma pena, pakuona kuti anaikiza kwa ine Uthenga Wabwino wa kusadulidwa, monga kwa Petro Uthenga Wabwino wa mdulidwe