Galatians 4:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chimene ndikufuna kunena ndi ichi: Mloŵachuma akali wamng'ono sasiyana ndi kapolo, ngakhale iyeyo ndi mwini chuma chonsecho.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ndinena kuti, pokhala wolowa nyumba ali wakhanda, sasiyana ndi kapolo, angakhale ali mwini zonse;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chimene ndikunena ndi chakuti, ngati mlowamʼmalo akali wamngʼono, sasiyana ndi kapolo, ngakhale kuti chuma chonse ndi chake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ndinena kuti, pokhala wolowa nyumba ali wakhanda, sasiyana ndi kapolo, angakhale ali mwini zonse;