Galatians 4:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Monga ndasanduka mdani wanu popeza kuti ndakuuzani zoona?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kotero kodi ndasanduka mdani wanu, pakukunenerani zoona?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi tsopano ine ndasanduka mdani wanu chifukwa ndakuwuzani choonadi?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kotero kodi ndasanduka mdani wanu, pakukunenerani zoona?