Galatians 4:29 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nthaŵi imeneyo mwana uja amene adaabadwa monga momwe amabadwira ana onseyu, ankasautsa mwana winayo wobadwa mwa mphamvu za Mzimu Woyera, ndipo mpaka tsopano zili chimodzimodzi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Komatu monga pompaja iye wobadwa monga mwa thupi anazunza wobadwa monga mwa Mzimu, momwemonso tsopano.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nthawi imeneyo mwana wobadwa mwathupi anazunza mwana wobadwa mwamphamvu za Mzimu. Zili chimodzimodzinso lero.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Komatu monga pompaja iye wobadwa monga mwa thupi anazunza wobadwa monga mwa Mzimu, momwemonso tsopano,