Galatians 5:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chimene ndikufuna kunena ndi ichi: Mulole Mzimu Woyera kuti azikutsogolerani. Mukatero, pamenepo simudzachita zimene khalidwe lanu lokonda zoipa limalakalaka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ndinena, Muyendeyende ndi Mzimu, ndipo musafitse chilakolako cha thupi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho ine ndikuti, mulole kuti Mzimu akutsogolereni ndipo simudzachita zofuna za thupi lanu la uchimo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ndinena, Muyendeyende ndi Mzimu, ndipo musafitse cilakolako ca thupi.