Galatians 5:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma ngati Mzimu Woyera akutsogolerani, ndiye kuti sindinunso akapolo a Malamulo a Mose.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati Mzimu akutsogolerani, simuli omvera lamulo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ngati Mzimu akutsogolerani, ndiye kuti simuli pansi pa lamulo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngati Mzimu akutsogolerani, simuli omvera lamulo.