Galatians 5:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngati Mzimu Woyera adatipatsa moyo, tilolenso kuti Mzimu yemweyo azititsogolera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati tili ndi moyo ndi Mzimu, ndi Mzimunso tiyende.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Popeza timakhala ndi moyo mwa Mzimu Woyera, tiyeni tiyende pamodzi ndi Mzimu Woyera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
1 N gati tiri ndi moyo ndi Mzimu, ndi Mzimunso tiyende.