Galatians 6:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tisatope nkuchita zabwino, chifukwa pa nthaŵi yake tidzakolola, ngati sitilefuka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma tisaleme pakuchita zabwino; pakuti pa nyengo yake tidzatuta tikapanda kufooka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tisatope nʼkuchita zabwino, pakuti pa nthawi yoyenera tidzakolola ngati sititopa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma tisaleme pakucita zabwino pakuti pa nyengo yace tidzatuta tikapanda kufoka.