Genesis 1:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Miyuni imeneyi ikhale ku thambo ndi kumaunikira dziko lapansi,” ndipo zidachitikadi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zikhale zounikira m'thambo la kumwamba, kuti ziunikire pa dziko lapansi: ndipo kunatero.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
zikhale kuthambo kuti ziwunikire pa dziko lapansi. Ndipo zinachitikadi.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
zikhale zounikira m'thambo la kumwamba, kuti ziunikire pa dziko lapansi; ndipo kunatero.