Genesis 1:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mulungu adaika miyuniyo ku thambo, kuti iziwunikira dziko lapansi,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mulungu ndipo adaika zimenezo m'thambo la kumwamba, kuti ziunikire pa dziko lapansi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mulungu anaziyika mlengalenga kuti ziziwunikira pa dziko lapansi,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mulungu ndipo adaika zimenezo m'thambo la kumwamba, kuti ziunikire pa dziko lapansi,