Genesis 10:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ana a Gomeri anali Asikenazi, Rifati ndi Togarima.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi ana amuna a Gomeri: Asikenazi, ndi Rifati, ndi Togarima.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi ana amuna a Gomeri: Asekenazo, ndi Rifata, ndi Togarma.