Genesis 11:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Serugi ali wa zaka 30, adabereka mwana dzina lake Nahori.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Serugi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Nahori:
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene Serugi anali ndi zaka makumi atatu, anabereka Nahori.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Serugi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Nahori: