Genesis 11:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nahori ali wa zaka 29, adabereka mwana dzina lake Tera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Nahori anakhala ndi moyo zaka makumi awiri kudza zisanu ndi zinai, nabala Tera:
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene Nahori anali ndi zaka 29, anabereka Tera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Nahori anakhala ndi moyo zaka makumi awiri kudza zisanu ndi zinai, nabala Tera: