Genesis 13:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Abramu anali wolemera kwambiri. Anali ndi zoŵeta monga: nkhosa, mbuzi ndi ng'ombe, ndiponso siliva ndi golide yemwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Abramu anali wolemera ndithu ndi ng'ombe ndi siliva ndi golide.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Abramu anali wolemera kwambiri; anali ndi ziweto ndiponso siliva ndi golide.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Abramu anali wolemera ndithu ndi ng'ombe ndi siliva ndi golidi,