Genesis 15:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Miphamba idadzatera kuti idye nyama zimene adaaphazo, koma Abramu adaipirikitsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamene miimba inatsikira panyama, Abramu anaingitsa iyo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene miphamba inabwera kuti itole nyama ija, Abramu anayipirikitsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamene miimba inatsikira panyama, Abramu anaingitsa iyo.