Genesis 18:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Apo Abrahamu adayandikira kwa Chauta namufunsa kuti, “Kodi monga mudzaonongadi anthu osachimwa pamodzi ndi ochimwa?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Abrahamu anayandikira nati, Kodi mudzaononga olungama pamodzi ndi oipa?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kenaka Abrahamu anasendera kufupi ndi Iye nati, “Kodi mudzawonongera kumodzi wolungama ndi woyipa?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Abrahamu anayandikira nati, Kodi mudzaononga olungama pamodzi ndi oipa?