Genesis 19:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono adaŵapempha kuti, “Inu abwenzi anga, musachite zimenezi chifukwa nkulakwa kwambiri kuchita zotere.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anati, Abale anga, musachitetu koipa kotere.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndipo anati, “Ayi anzanga, musachite zinthu zoyipa zotere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anati, Abale anga, musacitetu koipa kotere.