Genesis 2:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero dziko lonse lapansi, thambo ndi zonse zokhala m'menemo, zidatha kulengedwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo zinatha kupangidwa zakumwamba ndi dziko lapansi, ndi khamu lao lonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Motero kumwamba, dziko lapansi ndi zonse za mʼmenemo zinatha kulengedwa monga mwa kuchuluka kwawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo zinatha kupangidwa zakumwamba ndi dziko lapansi, ndi khamu lao lonse.