Genesis 2:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
(Golide wakumeneko ndi wabwino. Kumapezekanso bedeliyo ndi miyala ya mtengowapatali yotchedwa onikisi.)
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
golide wa dziko ali wabwino; ndimonso muli bedola ndi mwala wasohamu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
(Golide wa ku dziko ili ndi wabwino. Kulinso miyala yokongola ya bedola ndi onikisi).
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
golidi wa dziko ali wabwino; ndimonso muli bedola ndi mwala wasohamu.