Genesis 2:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwamunayo ndi mkazi wake uja, onse anali maliseche, komabe sankachita manyazi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Onse awiri ndipo anali amaliseche, mwamuna ndi mkazi wake, ndipo analibe manyazi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu uja ndi mkazi wakeyo, onse awiri anali maliseche ndipo analibe manyazi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Onse awiri ndipo anali amarisece, mwamuna ndi mkazi wace, ndipo analibe manyazi.