Genesis 20:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chifukwa chiyani wachita zimenezi?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Abimeleki anati kwa Abrahamu, Unaona chiyani iwe kuti wachita ichi?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo Abrahamu anafunsa Abimeleki kuti, “Chifukwa chiyani wachita zimenezi?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Abimeleke anati kwa Abrahamu, Unaona ciani iwe kuti wacita ici?