Genesis 21:34 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo adakhala m'dziko la Afilisti nthaŵi yaitali.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Abrahamu anakhala ngati mlendo masiku ambiri m'dziko la Afilisti.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo Abrahamu anakhala mʼdziko la Afilisti kwa nthawi yayitali.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Abrahamu anakhala ngati mlendo masiku ambiri m'dziko la Afilisti.