Genesis 23:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthuwo adamuyankha kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ana a Hiti anayankha Abrahamu nati kwa iye,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu a ku Hiti aja anamuyankha Abrahamu kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ana a Heti anayankha Abrahamu nati kwa iye,