Genesis 24:29 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Apo Labani, mlongo wa Rebekayo, adaonadi chipini chija pamodzi ndi zigwinjiri pa mikono ya mlongo wakeyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Rebeka anali ndi mlongo wake dzina lake Labani; ndipo Labani anathamangira munthuyo kunja ku kasupe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono Rebeka anali ndi mlongo wake dzina lake Labani.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Rebeka anali ndi mlongo wace dzina lace Labani; ndipo Labani anathamangira munthuyo kunja ku kasupe.