Genesis 24:42 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Tsono lero lino nditafika ku chitsime, ndinapemphera kuti, ‘Chauta, Mulungu wa mbuyanga Abrahamu, chonde mundithandize kuti ndikhoze pa ulendo wangawu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndinafika lero kukasupe, ndipo ndinati, Yehova Mulungu wa mbuyanga Abrahamu, ngati mundiyendetsatu bwino njira yanga m'mene ndinkamo ine;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Tsono lero lino pamene ndafika pa chitsime, ndinapempha kuti, ‘Yehova, Mulungu wa mbuye wanga, Abrahamu, ngati Inu mwandidalitsadi pa ulendowu,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndinafika lero kukasupe, ndipo ndinati, Yehova Mulungu wa mbuyanga Abrahamu, ngati mundiyendetsatu bwino njira yanga m'mene ndinkamo ine;