Genesis 25:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
(Ismaele anali wa zaka 137 pa nthaŵi imene ankamwalira, ndipo adaikidwa m'manda.)
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zaka za moyo wa Ismaele ndi izi: zaka zana limodzi kudza makumi atatu ndi zisanu ndi ziwiri: ndipo iye anamwalira, natengedwa akhale ndi a mtundu wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ismaeli anakhala ndi moyo zaka 137. Iye anamwalira ndipo anakakhala ndi anthu a mtundu wake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zaka za moyo wa Ismayeli ndi izi: zaka zana limodzi kudza makumi atatu ndi zisanu ndi ziwiri: ndipo iye anamwalira, natengedwa akhale ndi a mtundu wace.