Genesis 25:27 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anyamatawo adakula ndithu, ndipo Esau adasanduka mlenje wodziŵa kusaka nyama, wokonda kuyendayenda. Koma Yakobe anali wachete, wokonda kukhala kunyumba.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anakula anyamatawo; ndipo Esau anali munthu wakudziwa zakusaka nyama, munthu wa m'thengo; ndipo Yakobo anali munthu wofatsa, wakukhala m'mahema.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anyamatawo anakula ndipo Esau anakhala katswiri wosaka, munthu wamʼthengo, pamene Yakobo anali munthu wofatsa, wokonda kukhala pa nyumba.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anakula anyamatawo; ndipo Esau anali munthu wakudziwa zakusaka nyama, munthu wa m'thengo; ndipo Yakobo anali munthu wofatsa, wakukhala m'mahema.