Genesis 25:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Abrahamu adakhala ndi moyo zaka 175.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Masiku a zaka za moyo wake wa Abrahamu amene anakhala ndi moyo ndiwo zaka zana limodzi, kudza makumi asanu ndi limodzi, kudza khumi ndi zisanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Abrahamu anakhala ndi moyo zaka 175.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Masiku a zaka za moyo wace wa Abrahamu amene anakhala ndi moyo ndiwo zaka zana limodzi, kudza makumi asanu ndi limodzi, kudza khumi ndi zisanu.