Genesis 25:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adamwalira ali nkhalamba yotheratu, atagonera zaka zochuluka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Abrahamu anamwalira, nafa m'ukalamba wake wabwino, nkhalamba ya zaka zambiri; natengedwa akhale ndi a mtundu wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Abrahamu anamwalira atakalamba kwambiri ndipo anakakhala ndi anthu a mtundu wake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Abrahamu anamwalira, nafa m'ukalamba wace wabwino, nkhalamba ya zaka zambiri; natengedwa akhale ndi a mtundu wace.