Genesis 26:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Antchito a Isaki aja adakumba chitsime china, ndipo padaukanso mkangano wina pa za chitsime chimenecho. Motero adachitcha Chidani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anakumbanso chitsime china, ndipo anakangana nachonso; natcha dzina lake Sitina.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kenaka iwo anakumba chitsime china, koma anakangananso chifukwa cha chitsimecho. Choncho anachitcha dzina lakuti Chidani.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anakumbanso citsime cina, ndipo anakangana naconso; nacha dzina lace Sitina.