Genesis 26:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzakudalitsa iwe chifukwa Abrahamu adandimvera, ndipo adatsata malamulo ndi malangizo anga onse.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
chifukwa kuti Abrahamu anamvera mau anga, nasunga chilangizo changa, ndi maweruziro anga, ndi malemba anga ndi malamulo anga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
chifukwa Abrahamu anandimvera, nasunga malamulo anga onse.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
cifukwa kuti Abrahamu anamvera mau anga, nasunga cilangizo canga, ndi maweruziro anga, ndi malemba anga ndi malamulo anga.