Genesis 27:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Isakiyo adati, “Ona, ine nkukalamba kuno, ndipo sindidziŵa tsiku loti ndidzafe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anati, Taonatu, ndakalamba, sindidziwa tsiku la kufa kwanga:
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Isake anati, “Tsopano ine ndakalamba, ndipo sindidziwa tsiku langa lakufa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anati, Taonatu, ndakalamba, sindidziwa tsiku la kufa kwanga: