Genesis 27:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Rebeka adauza Yakobe kuti, “Ine ndamva bambo wako akuuza Esau kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Rebeka ananena kwa Yakobo mwana wake, nati, Taona ndinamva atate wako alimkunena ndi Esau mkulu wako kuti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Rebeka anati kwa mwana wake Yakobo, “Taona ndamva abambo ako akuwuza mʼbale wako Esau kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Rebeka ananena kwa Yakobo mwana wace, nati, Taona ndinamva atate wako alinkunena ndi Esau mkuru wako kuti,