Genesis 27:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndiye iwe mwana wanga, undimvere ndipo uchite zonse zimene ndikuuze.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tsopanotu mwana wanga, tamvera mau anga monga momwe nditi ndikuuze iwe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsopano mwana wanga, mvetsetsa ndipo uchite zimene ndikuwuze:
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tsopanotu mwana wanga, tamvera mau anga monga momwe nditi ndikuuze iwe.