Genesis 29:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Labani adauza Yakobe kuti, “Suyenera kundigwirira ntchito popanda malipiro, chifukwa choti ndife abale. Undiwuze zimene ukufuna kuti ndikulipire.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Labani anati kwa Yakobo, Chifukwa iwe ndiwe mbale wanga, kodi udzanditumikira ine kwachabe? Undiuze ine, malipiro ako adzakhala otani?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono Labani anawuza Yakobo kuti, “Zoona iwe ndi ife ndi abale. Koma suyenera kundigwirira ntchito popanda malipiro. Ndiwuze kuti malipiro ako azikhala wotani?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Labani anati kwa Yakobo, Cifukwa iwe ndiwe mbale wanga, kodi udzanditumikira ine kwacabe? Undiuze ine, malipiro ako adzakhala otani?