Genesis 29:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yakobe ankakonda Rakele, ndipo adati, “Ndidzakugwirirani ntchito zaka zisanu ndi ziŵiri chifukwa cha mwana wanu Rakele.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yakobo anamkonda Rakele, nati, Ndidzakutumikirani inu zaka zisanu ndi ziwiri chifukwa cha Rakele mwana wanu wamkazi wamng'ono.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yakobo anakonda Rakele ndipo anati, “Ndidzakugwirirani ntchito kwa zaka zisanu ndi ziwiri chifukwa cha mwana wanu wamngʼono, Rakele.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yakobo anamkonda Rakele, nati, Ndidzakutumikirani inu zaka zisanu ndi ziwiri cifukwa ca Rakele mwana wanu wamkazi wamng'ono.