Genesis 3:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Chauta adamuitana Adamu uja kuti, “Kodi uli kuti?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yehova Mulungu anaitana mwamunayo nati kwa iye, Uli kuti?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova Mulungu anayitana munthu uja kuti, “Uli kuti?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yehova Mulungu anaitana mwamunayo nati kwa iye, Uli kuti?