Genesis 30:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Atabadwa Yosefe, Yakobe adauza Labani kuti, “Mundilole ndizibwerera kwathu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo panali pamene Rakele anabala Yosefe, Yakobo anati kwa Labani, Undisudzule ine ndinke kwathu ku dziko langa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Rakele atabereka Yosefe, Yakobo anati kwa Labani, “Ndimasuleni kuti ndizipita ku dziko la kwathu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo panali pamene Rakele anabala Yosefe, Yakobo anati kwa Labani, Undisudzule ine ndinke kwathu ku dziko langa.