Genesis 30:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Biliha adatenga pathupi namubalira Yakobe mwana wamwamuna.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Biliha anatenga pakati, nambalira Yakobo mwana wamwamuna.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndipo Bilihayo anatenga pathupi namubalira Yakobo mwana wamwamuna.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Biliha anatenga pakati, nambalira Yakobo mwana wamwamuna.